Luka 24:38 - Buku Lopatulika38 Ndipo anati kwa iwo, Mukhala bwanji ovutika? Ndipo matsutsano amauka bwanji m'mtima mwanu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Ndipo anati kwa iwo, Mukhala bwanji ovutika? Ndipo matsutsano amauka bwanji m'mtima mwanu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Tsono Yesu adati, “Mukuvutikiranji, mukudzipheranji ndi mafunso m'mitima mwanu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Iye anawafunsa kuti, “Nʼchifukwa chiyani mukuvutika? Nʼchifukwa chiyani mukukayika mu mtima mwanu? Onani mutuwo |