Luka 24:36 - Buku Lopatulika36 Ndipo pakulankhula izi iwowa, Iye anaimirira pakati pao; nanena nao, Mtendere ukhale nanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Ndipo pakulankhula izi iwowa, Iye anaimirira pakati pao; nanena nao, Mtendere ukhale nanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Iwo akulankhula choncho, Yesu mwiniwake adadzaimirira pakati pao nati, “Mtendere ukhale nanu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Akufotokoza zimenezi, Yesu mwini wake anayimirira pakati pawo ndipo anati, “Mukhale ndi mtendere.” Onani mutuwo |