Luka 24:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo anayandikira kumudzi umene analikupitako; ndipo anachita ngati anafuna kupitirira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo anayandikira kumudzi umene analikupitako; ndipo anachita ngati anafuna kupitirira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Atayandikira kumudzi kumene ankapita, Yesu adachita ngati akupitirira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Atayandikira mudzi omwe amapitako, Yesu anachita ngati akupitirira. Onani mutuwo |