Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 24:28 - Buku Lopatulika

28 Ndipo anayandikira kumudzi umene analikupitako; ndipo anachita ngati anafuna kupitirira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Ndipo anayandikira kumudzi umene analikupitako; ndipo anachita ngati anafuna kupitirira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Atayandikira kumudzi kumene ankapita, Yesu adachita ngati akupitirira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Atayandikira mudzi omwe amapitako, Yesu anachita ngati akupitirira.

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:28
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anati, Taonanitu, Ambuye anga, tembenukanitu, kulowa m'nyumba mwa kapolo wanu, mugone usiku wonse, mutsuke mapazi anu, ndipo mudzalawira m'mawa kunka ulendo wanu. Ndipo anati, Iai; koma tigone m'khwalalamu usiku wonse.


Ndipo iye anati Ndileke ndimuke, chifukwa kulinkucha. Ndipo Yakobo anati, Sindidzakuleka iwe kuti umuke, ukapanda kundidalitsa ine.


Ndipo Yosefe anaona abale ake, ndipo anazindikira iwo, koma anadziyesetsa kwa iwo ngati mlendo, nanena kwa iwo mwankhanza: ndipo anati kwa iwo, Mufuma kuti inu? Nati iwo, Ku dziko la Kanani kudzagula chakudya.


Ndipo pakuwaona ali kuvutidwa ndi kupalasa, pakuti mphepo inadza nikomana nao, pa ulonda wachinai wa usiku Iye anadza kwa iwo, alikuyenda pamwamba pa nyanja; nati awapitirire;


Ndipo anamuumiriza Iye, nati, Khalani ndi ife; pakuti kuli madzulo, ndipo dzuwa lapendekatu. Ndipo analowa kukhala nao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa