Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 23:49 - Buku Lopatulika

49 Ndipo omdziwa Iye onse, ndi akazi amene adamtsata kuchokera ku Galileya, anaima kutali, naona zinthu izi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

49 Ndipo omdziwa Iye onse, ndi akazi amene adamtsata kuchokera ku Galileya, anaima kutali, naona zinthu izi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

49 Anthu onse amene ankadziŵana ndi Yesu, ndiponso azimai amene adaamtsatira kuchokera ku Galileya, adaima patali nkumaona zimenezi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

49 Koma onse amene anamudziwa Iye, kuphatikiza amayi amene anamutsatira kuchokera ku Galileya, anayimirira akuona zinthu izi.

Onani mutuwo Koperani




Luka 23:49
12 Mawu Ofanana  

Iye anandichotsera abale anga kutali, ndi odziwana nane andiyesa mlendo konse.


Penyani kudzanja lamanja ndipo muone; palibe wondidziwa; pothawirapo pandisowa; palibe mmodzi wosamalira moyo wanga.


Ondikonda ndi anzanga apewa mliri wanga; ndipo anansi anga aima patali.


Munandichotsera kutali wondikonda ndi bwenzi langa, odziwana nane akhala kumdima.


Ndipo Maria wa Magadala anali pamenepo, ndi Maria winayo, anakhala pansi popenyana ndi mandawo.


Ndipo Maria wa Magadala ndi Maria amake wa Yosefe anapenya pomwe anaikidwapo.


Ndipo unamtsata unyinji waukulu wa anthu, ndi wa akazi amene anadziguguda pachifuwa, namlirira Iye.


Ndipo akazi, amene anachokera naye ku Galileya, anatsata m'mbuyo, naona manda, ndi maikidwe a mtembo wake.


ndi akazi ena amene anachiritsidwa ziwanda ndi nthenda zao, ndiwo, Maria wonenedwa Magadala, amene ziwanda zisanu ndi ziwiri zinatuluka mwa iye,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa