Luka 23:48 - Buku Lopatulika48 Ndipo makamu onse osonkhana kudzapenya ichi, pamene anaona zinachitikazo, anapita kwao ndi kudziguguda pachifuwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 Ndipo makamu onse osonkhana kudzapenya ichi, pamene anaona zinachitikazo, anapita kwao ndi kudziguguda pachifuwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 Anthu onse amene adaasonkhana kudzaonerera zimene zinkachitikazo, ataona zonsezi, adabwerera kwao akudzigunda pa chifuwa ndi chisoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 Anthu onse amene anasonkhana kudzaonerera izi, ataona zinachitikazo, anadziguguda pachifuwa ndipo anachoka. Onani mutuwo |