Luka 23:45 - Buku Lopatulika45 Ndipo nsalu yotchinga ya mu Kachisi inang'ambika pakati. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201445 Ndipo nsalu yotchinga ya m'Kachisi inang'ambika pakati. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa45 dzuŵa litangoti bii kuda. Pamenepo chinsalu chochinga chija cha m'Nyumba ya Mulungu chidang'ambika pakatimpakati. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero45 pakuti dzuwa linaleka kuwala. Ndipo chinsalu cha mʼNyumba ya Mulungu chinangʼambika pakati. Onani mutuwo |