Luka 23:43 - Buku Lopatulika43 Ndipo Iye ananena naye, Indetu, ndinena ndi iwe, Lero lino udzakhala ndine mu Paradaiso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Ndipo Iye ananena naye, Indetu, ndinena ndi iwe, Lero lino udzakhala ndine m'Paradaiso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Yesu adamuyankha kuti, “Ndithu ndikunenetsa kuti lero lomwe lino ukhala nane ku Malo a Chisangalalo, Kumwamba.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Yesu anayankha kuti, “Zoonadi, ndikukuwuza kuti lero lino udzakhala ndi Ine mʼparadaiso.” Onani mutuwo |