Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 23:39 - Buku Lopatulika

39 Ndipo mmodzi wa ochita zoipa anapachikidwawo anamchitira Iye mwano nanena, Kodi suli Khristu Iwe? Udzipulumutse wekha ndi ife.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 Ndipo mmodzi wa ochita zoipa anapachikidwawo anamchitira Iye mwano nanena, Kodi suli Khristu Iwe? Udzipulumutse wekha ndi ife.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 Chigaŵenga chimodzi chimene chidaapachikidwa nao, chidayamba kunyoza Yesu nkumanena kuti, “Ha! Kodi iwe sindiwe Mpulumutsi Wolonjezedwa uja? Udzipulumutse wekha ndi ife tomwe.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 Mmodzi wa achifwambawo, amene anapachikidwa, anamunenera Iye zamwano nati, “Kodi sindiwe Khristu? Dzipulumutse wekha ndi ifenso!”

Onani mutuwo Koperani




Luka 23:39
6 Mawu Ofanana  

Ndiponso achifwambawo opachikidwa pamodzi ndi Iye, anamlalatira Iye mau amodzimodzi.


Atsike tsopano pamtanda, Khristu mfumu ya Israele, kuti tione, ndi kukhulupirira. Ndipo iwo akupachikidwa naye anamlalatira.


Ndipo anthu anaima alikupenya. Ndi akulunso anamlalatira Iye, nanena, Anapulumutsa ena; adzipulumutse yekha ngati iye ndiye Khristu wa Mulungu, wosankhidwa wake.


nanena, Ngati Iwe ndiwe mfumu ya Ayuda, udzipulumutse wekha.


Koma winayo anayankha, namdzudzula iye, nati, Kodi suopa Mulungu, poona uli m'kulangika komweku?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa