Luka 23:36 - Buku Lopatulika36 Ndipo asilikalinso anamnyoza, nadza kwa Iye, nampatsa vinyo wosasa, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Ndipo asilikalinso anamnyoza, nadza kwa Iye, nampatsa vinyo wosasa, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Nawonso asilikali adayamba kumseka. Adadza pafupi ndi Iye, nampatsa vinyo wosasa kuti amwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Asilikalinso anabwera ndi kumunyoza Iye. Iwo anamupatsa vinyo wosasa, Onani mutuwo |