Luka 23:32 - Buku Lopatulika32 Ndipo analinso awiri ena, ndiwo ochita zoipa, anatengedwa pamodzi ndi Iye kuti aphedwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ndipo analinso awiri ena, ndiwo ochita zoipa, anatengedwa pamodzi ndi Iye kuti aphedwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Asilikali aja adaatenganso anthu ena aŵiri, amene anali zigaŵenga, kuti akaphedwe pamodzi ndi Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Amuna ena awiri, onsewo achifwamba, anatengedwanso pamodzi ndi Yesu kukaphedwa. Onani mutuwo |