Luka 23:31 - Buku Lopatulika31 Pakuti ngati azichitira izi mtengo wauwisi, nanga kudzatani ndi wouma? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Pakuti ngati azichitira izi mtengo wauwisi, nanga kudzatani ndi wouma? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Pakuti ngati mtengo wauŵisi auchita zimenezi, nanga mtengo wouma ndiye adzauchita zotani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Chifukwa ngati anthu akuchita izi pa mtengo wauwisi, chidzachitike nʼchiyani ndi wowuma?” Onani mutuwo |
Ndipo atapita masabata makumi asanu ndi limodzi mphambu awiri wodzozedwayo adzalikhidwa, nadzakhala wopanda kanthu; ndi anthu a kalonga wakudzayo adzaononga mzinda ndi malo opatulika; ndi kutsiriza kwake kudzakhala kwa chigumula, ndi kufikira chimaliziro kudzakhala nkhondo; chipasuko chalembedweratu.