Luka 23:30 - Buku Lopatulika30 Pomwepo adzayamba kunena kwa mapiri, Igwani pa ife; ndi kwa zitunda, Bisani ife. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Pomwepo adzayamba kunena kwa mapiri, Igwani pa ife; ndi kwa zitunda, Bisani ife. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Nthaŵi imeneyo adzapempha mapiri kuti, ‘Tigwereni,’ ndiponso magomo kuti, ‘Tiphimbeni.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Kenaka, “adzawuza mapiri kuti tigwereni ife; zitunda kuti tiphimbeni ife. Onani mutuwo |