Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 23:30 - Buku Lopatulika

30 Pomwepo adzayamba kunena kwa mapiri, Igwani pa ife; ndi kwa zitunda, Bisani ife.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Pomwepo adzayamba kunena kwa mapiri, Igwani pa ife; ndi kwa zitunda, Bisani ife.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Nthaŵi imeneyo adzapempha mapiri kuti, ‘Tigwereni,’ ndiponso magomo kuti, ‘Tiphimbeni.’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Kenaka, “adzawuza mapiri kuti tigwereni ife; zitunda kuti tiphimbeni ife.

Onani mutuwo Koperani




Luka 23:30
6 Mawu Ofanana  

Anthu adzalowa m'mapanga a m'matanthwe, ndi m'maenje apansi, kuthawa kuopsa kwa Yehova, ndi ulemerero wachifumu wake, podzuka Iye kugwedeza dziko ndi mphamvu.


Tsiku limenelo munthu adzataya kumfuko ndi kumileme mafano ake asiliva ndi agolide amene anthu anampangira iye awapembedze;


Ndipo misanje ya Aveni, ndiyo tchimo la Israele, idzaonongeka; minga ndi mitungwi idzamera pa maguwa ao a nsembe; ndipo adzati kwa mapiri, Tiphimbeni; ndi kwa zitunda, Tigwereni.


Pakuti ngati azichitira izi mtengo wauwisi, nanga kudzatani ndi wouma?


nanena kwa mapiri ndi matanthwe, Igwani pa ife, ndipo tibiseni ife kunkhope ya Iye amene akhala pa mpando wachifumu, ndi kumkwiyo wa Mwanawankhosa;


Ndipo m'masiku ajawo, anthu adzafunafuna imfa osaipeza konse; ndipo adzakhumba kumwalira, koma imfa idzawathawa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa