Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 23:21 - Buku Lopatulika

21 koma iwo anafuula, nanena, Mpachikeni, mpachikeni pamtanda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 koma iwo anafuula, nanena, Mpachikeni, mpachikeni pamtanda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Koma iwo adafuulirafuulira kuti, “Mpachikeni! Mpachikeni!”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Koma iwo anapitirirabe kufuwula kuti, “Mpachikeni! Mpachikeni!”

Onani mutuwo Koperani




Luka 23:21
7 Mawu Ofanana  

Ndipo anafuulanso, Mpachikeni pamtanda.


Ndipo Pilato analankhulanso nao, nafuna kumasula Yesu;


Ndipo anati kwa iwo nthawi yachitatu, Nanga munthuyu anachita choipa chiyani? Sindinapeze chifukwa cha kufera Iye; chotero ndidzamkwapula Iye ndi kummasula.


Koma anakakamiza ndi mau okweza, napempha kuti Iye apachikidwe. Ndipo mau ao anapambana.


Pamenepo anafuula iwowa, Chotsani, Chotsani, mpachikeni Iye! Pilato ananena nao, Ndipachike mfumu yanu kodi? Ansembe aakulu anayankha, Tilibe mfumu koma Kaisara.


Ndipo ngakhale sanapeze chifukwa cha kumphera, anapempha Pilato kuti aphedwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa