Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 23:20 - Buku Lopatulika

20 Ndipo Pilato analankhulanso nao, nafuna kumasula Yesu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Ndipo Pilato analankhulanso nao, nafuna kumasula Yesu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Pilato adafuna kumasula Yesu, motero adakakamba nawonso anthu aja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Pofuna kumumasula Yesu, Pilato anawadandaulira iwo.

Onani mutuwo Koperani




Luka 23:20
6 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Pilato analikukhala pa mpando wakuweruza, mkazi wake anatumiza mau kwa iye, kunena, Musachite kanthu ndi munthu wolungamayo; pakuti lero m'kulota ine ndasauka kwambiri chifukwa cha Iye.


Ndipo Pilato pofuna kuwakhazika mtima anthuwo, anawamasulira Barabasi, napereka Yesu, atamkwapula, akampachike pamtanda.


ndiye munthu anaponyedwa m'ndende chifukwa cha mpanduko m'mzinda ndi cha kupha munthu.


koma iwo anafuula, nanena, Mpachikeni, mpachikeni pamtanda.


Pa ichi Pilato anafuna kumasula Iye; koma Ayuda anafuula, ndi kunena, Ngati mumasula ameneyo, simuli bwenzi la Kaisara; yense wodziyesera yekha mfumu atsutsana naye Kaisara.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa