Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 22:65 - Buku Lopatulika

65 Ndipo zambiri zina anamnenera Iye, namchitira mwano.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

65 Ndipo zambiri zina anamnenera Iye, namchitira mwano.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

65 Ndipo adamnenanso mau ena ambiri achipongwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

65 Ndipo iwo anamunena zachipongwe zambiri.

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:65
6 Mawu Ofanana  

Ndipo anthu akupitirirapo anamchitira mwano Iye ndi kupukusa mitu yao,


Ndipo onani, ena a alembi ananena mumtima mwao, Uyu achitira Mulungu mwano.


Ndipo aliyense amene adzanenera Mwana wa Munthu zoipa adzakhululukidwa; koma amene anenera Mzimu Woyera zamwano sadzakhululukidwa.


Ndipo ndinawalanga kawirikawiri m'masunagoge onse, ndi kuwakakamiza anene zamwano; ndipo pakupsa mtima kwakukulu pa iwo ndinawalondalonda ndi kuwatsata ngakhale kufikira kumizinda yakunja.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa