Luka 22:64 - Buku Lopatulika64 Ndipo anamkulunga Iye m'maso, namfunsa, nati, Talota; anakupanda Iwe ndani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201464 Ndipo anamkulunga Iye m'maso, namfunsa, nati, Talota; anakupanda Iwe ndani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa64 Adammanga nsalu m'maso nkumamufunsa kuti, “Lota, wakumenya ndani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero64 Anamumanga mʼmaso ndi kumufunsa kuti, “Tanenera! Wakumenya iwe ndi ndani?” Onani mutuwo |