Luka 22:62 - Buku Lopatulika62 Ndipo anatuluka, nalira misozi ndi kuwawa mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201462 Ndipo anatuluka, nalira misozi ndi kuwawa mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa62 Pamenepo adatuluka, nakalira kwambiri chifukwa cha chisoni chachikulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero62 Ndipo iye anapita panja nakalira kwambiri. Onani mutuwo |