Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 22:58 - Buku Lopatulika

58 Ndipo popita kamphindi, anamuona wina, nati, Iwenso uli mmodzi wa awo. Koma Petro anati, Munthu iwe, sindine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

58 Ndipo popita kamphindi, anamuona wina, nati, Iwenso uli mmodzi wa awo. Koma Petro anati, Munthu iwe, sindine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

58 Patapita kanthaŵi pang'ono, munthu wina pomuwona adati, “Akulu inu, ndinunso mmodzi mwa iwo aja.” Koma Petro adati, “Munthu iwe, ai ndithu sindine.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

58 Patatha kanthawi pangʼono, wina wake anamuona ndipo anati, “Iwenso ndiwe mmodzi mwa iwo.” Petro anayankha kuti, “Munthu iwe, ayi sindine.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:58
5 Mawu Ofanana  

Koma anakana, nati, Mkaziwe, sindimdziwa Iye.


Koma Simoni Petro analikuimirira ndi kuotha moto. Pomwepo anati kwa iye, Suli iwenso wa ophunzira ake kodi? Iyeyu anakana, nati, Sindine.


Mmodzi wa akapolo a mkulu wa ansembe ndiye mbale wake uja amene Petro anamdula khutu, ananena, Ine sindinakuone iwe kodi m'munda pamodzi ndi Iye?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa