Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 22:50 - Buku Lopatulika

50 Ndipo wina wa iwo anakantha kapolo wa mkulu wa ansembe, namdula khutu lake lamanja.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

50 Ndipo wina wa iwo anakantha kapolo wa mkulu wa ansembe, namdula khutu lake lamanja.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

50 Apo mmodzi mwa iwo adatemadi wantchito wa mkulu wa ansembe onse, mpaka kumusenga khutu la ku dzanja lamanja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

50 Ndipo mmodzi wa iwo anatema wantchito wamkulu wa ansembe, nadula khutu lake lamanja.

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:50
7 Mawu Ofanana  

Koma mmodzi wina wa iwo akuimirirapo, anasolola lupanga lake, nakantha kapolo wake wa mkulu wa ansembe, namdula khutu lake.


Ndipo m'mene iwo akumzinga Iye anaona chimene chiti chichitike, anati, Ambuye, tidzakantha ndi lupanga kodi?


Koma Yesu anayankha nati, Lolani kufikira kumene. Ndipo anakhudza khutu lake, namchiritsa.


Musabwezere choipa, okondedwa, koma patukani pamkwiyo; pakuti kwalembedwa, Kubwezera kuli kwanga, Ine ndidzabwezera, ati Ambuye.


(pakuti zida za nkhondo yathu sizili za thupi, koma zamphamvu mwa Mulungu zakupasula malinga);


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa