Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 22:49 - Buku Lopatulika

49 Ndipo m'mene iwo akumzinga Iye anaona chimene chiti chichitike, anati, Ambuye, tidzakantha ndi lupanga kodi?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

49 Ndipo m'mene iwo akumzinga Iye anaona chimene chiti chichitike, anati, Ambuye, tidzakantha ndi lupanga kodi?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

49 Ophunzira amene anali pafupi ndi Yesu ataona zimene zinalikudzachitika, adafunsa Yesu kuti, “Ambuye, kodi tiŵateme ndi lupanga?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

49 Otsatira Yesu ataona zimene zimati zichitike, anati, “Ambuye, kodi timenyane ndi malupanga athu?”

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:49
3 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo anati, Ambuye, taonani, malupanga awiri siwa. Ndipo anati kwa iwo, Chakwanira.


Koma Yesu anati kwa iye, Yudasi, ulikupereka Mwana wa Munthu ndi chimpsompsono kodi?


Ndipo wina wa iwo anakantha kapolo wa mkulu wa ansembe, namdula khutu lake lamanja.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa