Luka 22:45 - Buku Lopatulika45 Ndipo pamene ananyamuka pakupemphera anadza kwa ophunzira, nawapeza ali m'tulo ndi chisoni, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201445 Ndipo pamene ananyamuka pakupemphera anadza kwa ophunzira, nawapeza ali m'tulo ndi chisoni, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa45 Atapemphera, adaimirira napita kwa ophunzira ake. Adaŵapeza ali m'tulo chifukwa cha chisoni, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero45 Iye atamaliza kupemphera, ndi kubwerera kwa ophunzira ake, anawapeza atagona atafowoka ndi chisoni. Onani mutuwo |