Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 22:28 - Buku Lopatulika

28 Koma inu ndinu amene munakhala ndi Ine chikhalire m'mayesero anga;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Koma inu ndinu amene munakhala ndi Ine chikhalire m'mayesero anga;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 “Inu ndinu amene mwakhala ndi Ine pa masautso anga onse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Inu ndinu amene mwayima nane mʼmayesero.

Onani mutuwo Koperani




Luka 22:28
7 Mawu Ofanana  

Koma iye wakulimbika chilimbikire kufikira kuchimaliziro, yemweyo adzapulumuka.


Chifukwa chake Yesu ananena kwa Ayuda aja adakhulupirira Iye, Ngati mukhala inu m'mau anga, muli ophunzira anga ndithu;


alowe malo a utumiki uwu ndi utumwi, kuchokera komwe Yudasi anapatukira, kuti apite kumalo a iye yekha.


Pakuti popeza adamva zowawa, poyesedwa yekha, akhoza kuthandiza iwo amene ayesedwa.


Pakuti sitili naye mkulu wa ansembe wosatha kumva chifundo ndi zofooka zathu; koma wayesedwa m'zonse monga momwe ife, koma wopanda uchimo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa