Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 21:28 - Buku Lopatulika

28 Koma poyamba kuchitika izi weramukani, tukulani mitu yanu; chifukwa chiomboledwe chanu chayandikira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Koma poyamba kuchitika izi weramukani, tukulani mitu yanu; chifukwa chiomboledwe chanu chayandikira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Zimenezi zikadzayamba kuchitika, mudzaimirire nkukweza mitu yanu, chifukwa chipulumutso chanu chayandikira.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Zinthu izi zikadzayamba kuchitika, mudzayimirire ndi kutukula mitu yanu, chifukwa chipulumutso chanu chayandikira.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 21:28
11 Mawu Ofanana  

Ndipo mkazi anali nao mzimu wakumdwalitsa zaka khumi ndi zisanu ndi zitatu; nakhala wopeteka, ndimo analibe mphamvu konse yakuweramuka.


Ndipo kodi Mulungu sadzachitira chilungamo osankhidwa ake akumuitana usana ndi usiku, popeza aleza nao mtima?


Ndipo ananena nao fanizo; Onani mkuyu, ndi mitengo yonse:


Pakuti chiyembekezetso cha cholengedwa chilindira vumbulutso la ana a Mulungu.


Ndipo si chotero chokha, koma ife tomwe, tili nazo zipatso zoyamba za Mzimu, inde ifenso tibuula m'kati mwathu, ndi kulindirira umwana wathu, ndiwo chiomboledwe cha thupi lathu.


ndiye chikole cha cholowa chathu, kuti akeake akaomboledwe, ndi kuti ulemerero wake uyamikike.


Ndipo musamvetse chisoni Mzimu Woyera wa Mulungu, amene munasindikizidwa chizindikiro mwa Iye, kufikira tsiku la maomboledwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa