Luka 21:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo pamenepo adzaona Mwana wa Munthu alinkudza mu mtambo ndi mphamvu ndi ulemerero waukulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo pamenepo adzaona Mwana wa Munthu alinkudza mu mtambo ndi mphamvu ndi ulemerero waukulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Pamenepo anthu adzaona Mwana wa Munthu akubwera pa mitambo, ali ndi mphamvu ndi ulemerero waukulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Nthawi imeneyo adzaona Mwana wa Munthu akubwera ndi mitambo, mphamvu ndi ulemerero waukulu. Onani mutuwo |