Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 20:39 - Buku Lopatulika

39 Ndipo alembi ena anayankha nati, Mphunzitsi, mwanena bwino.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 Ndipo alembi ena anayankha nati, Mphunzitsi, mwanena bwino.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 Apo ena mwa aphunzitsi a Malamulo adauza Yesu kuti, “Aphunzitsi, mwanena bwino.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 Ena mwa aphunzitsi amalamulo anayankha kuti, “Mwanena bwino mphunzitsi!”

Onani mutuwo Koperani




Luka 20:39
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye sakhala Mulungu wa akufa, koma wa amoyo: pakuti anthu onse akhala ndi moyo kwa Iye.


Pakuti sanalimbenso mtima kumfunsa Iye kanthu kena.


Ndipo chidauka chipolowe chachikulu, ndipo alembi ena a kwa Afarisi anaimirira, natsutsana, nanena, Sitipeza choipa chilichonse mwa munthuyu; ndipo nanga bwanji ngati mzimu kapena mngelo walankhula naye?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa