Luka 20:38 - Buku Lopatulika38 Ndipo Iye sakhala Mulungu wa akufa, koma wa amoyo: pakuti anthu onse akhala ndi moyo kwa Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Ndipo Iye sakhala Mulungu wa akufa, koma wa amoyo: pakuti anthu onse akhala ndi moyo kwa Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Ndiye kutitu sali Mulungu wa anthu akufa ai, koma wa anthu amoyo, chifukwa kwa Iye anthu onsewo ndi amoyo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Mulungu si Mulungu wa akufa, koma wa amoyo, pakuti kwa Iye onse ali ndi moyo.” Onani mutuwo |