Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 19:48 - Buku Lopatulika

48 ndipo sanapeze chimene akachita; pakuti anthu onse anamlendewera Iye kuti amve.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

48 ndipo sanapeze chimene akachita; pakuti anthu onse anamlendewera Iye kuti amve.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

48 koma adaasoŵa chochita, chifukwa anthu onse ankatengeka nawo mtima mau ake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

48 Komabe iwo sanathe kupeza njira ina iliyonse kuti achite izi, chifukwa anthu onse anakhulupirira mawu ake.

Onani mutuwo Koperani




Luka 19:48
8 Mawu Ofanana  

Nawerenga m'menemo pa khwalala lili ku Chipata cha Madzi kuyambira mbandakucha kufikira msana, pamaso pa amuna ndi akazi, ndi iwo okhoza kuzindikira; ndi anthu onse anatcherera khutu buku la chilamulo.


Ndipo analikuphunzitsa mu Kachisi tsiku ndi tsiku. Koma ansembe aakulu, ndi alembi ndi akulu a anthu anafunafuna kumuononga Iye;


Ndipo kunali lina la masiku ao m'mene Iye analikuphunzitsa anthu mu Kachisi, ndi kulalikira Uthenga Wabwino, adamdzera ansembe aakulu ndi alembi pamodzi ndi akulu;


Ndipo anatimva mkazi wina dzina lake Lidia, wakugulitsa chibakuwa, wa kumzinda wa Tiatira, amene anapembedza Mulungu; mtima wake Ambuye anatsegula; kuti amvere zimene anazinena Paulo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa