Luka 19:46 - Buku Lopatulika46 Kwalembedwa, Ndipo nyumba yanga idzakhala nyumba yakupemphera; koma inu mwaiyesa phanga la achifwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201446 Kwalembedwa, Ndipo nyumba yanga idzakhala nyumba yakupemphera; koma inu mwaiyesa phanga la achifwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa46 Adaŵauza kuti, “Malembo akuti, ‘Nyumba yanga idzakhala nyumba yopemphereramo.’ Koma inu mwaisandutsa phanga la achifwamba.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero46 Iye anawawuza kuti, “Zinalembedwa kuti Nyumba yanga idzakhala nyumba ya mapemphero, koma inu mwayisadutsa phanga la achifwamba.” Onani mutuwo |