Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 19:45 - Buku Lopatulika

45 Ndipo analowa mu Kachisi, nayamba kutulutsa iwo akugulitsa malonda, nanena nao,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

45 Ndipo analowa m'Kachisi, nayamba kutulutsa iwo akugulitsa malonda, nanena nao,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

45 Yesu adaloŵa m'Nyumba ya Mulungu, nayamba kutulutsa anthu amene ankachita malonda m'menemo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

45 Kenaka Iye analowa mʼdera la Nyumba ya Mulungu ndi kuyamba kutulutsa kunja amene amachita malonda.

Onani mutuwo Koperani




Luka 19:45
4 Mawu Ofanana  

Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa