Luka 19:43 - Buku Lopatulika43 Pakuti masiku adzakudzera, ndipo adani ako adzakuzingira linga, nadzakuzungulira iwe kwete, nadzakutsekereza ponsepo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Pakuti masiku adzakudzera, ndipo adani ako adzakuzingira linga, nadzakuzungulira iwe kwete, nadzakutsekereza ponsepo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Nthaŵi idzakufikira pamene adani ako adzakuzinga ndi machemba, nadzakuzungulira, nkukutsekereza ponseponse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Pakuti masiku adzabwera pamene adani ako adzamanga mitumbira yankhondo nakuzungulira, nadzakutsekereza mbali zonse. Onani mutuwo |