Luka 19:42 - Buku Lopatulika42 nanena, Ukadazindikira tsiku ili, inde iwetu zinthu za mtendere! Koma tsopano zibisika pamaso pako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 nanena, Ukadazindikira tsiku ili, inde iwetu zinthu za mtendere! Koma tsopano zibisika pamaso pako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 Adati, “Ha, iwenso ukadangodziŵa lero lino zinthu zopatsa mtendere! Koma ai, tsopano maso ako sangathe kuziwona. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 nati, “Iwe ukanadziwa lero lino zinthu zokubweretsera mtendere, koma tsopano zabisikira maso ako. Onani mutuwo |