Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 19:40 - Buku Lopatulika

40 Ndipo anayankha nati, Ndinena ndi inu, ngati awa khala chete miyala idzafuula.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

40 Ndipo anayankha nati, Ndinena ndi inu, ngati awa khala chete miyala idzafuula.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

40 Iye adati, “Ndikutitu iwoŵa akangokhala chete, ifuula ndi miyalayi.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

40 Iye anayankha kuti, “Ine ndikukuwuzani kuti, ngati atakhala chete, miyala idzafuwula.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 19:40
11 Mawu Ofanana  

Kumwamba kukondwere nilisekerere dziko lapansi; nyanja ibume mwa kudzala kwake.


Pakuti inu mudzatuluka ndi kukondwa, ndi kutsogozedwa ndi mtendere; mapiri ndi zitunda, zidzaimba zolimba pamaso panu, ndi mitengo yonse ya m'thengo idzaomba m'manja mwao.


Pakuti mwala wa m'khoma ufuula, ndi mtanda wa kuphaso udzauvomereza.


Ndipo ora lachisanu ndi chimodzi panali mdima padziko lonse, kufikira ora lachisanu ndi chinai.


ndipo musamayesa kunena mwa inu nokha, Atate wathu tili naye Abrahamu; pakuti ndinena kwa inu kuti mwa miyala iyi Mulungu akhoza kuukitsira Abrahamu ana.


Ndipo m'mene anayandikira, anaona mzindawo naulirira,


ndipo pakuisandutsa makala mizinda ya Sodomu ndi Gomora anaitsutsa poigwetsa, ataiika chitsanzo cha kwa iwo akakhala osapembedza;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa