Luka 19:40 - Buku Lopatulika40 Ndipo anayankha nati, Ndinena ndi inu, ngati awa khala chete miyala idzafuula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Ndipo anayankha nati, Ndinena ndi inu, ngati awa khala chete miyala idzafuula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Iye adati, “Ndikutitu iwoŵa akangokhala chete, ifuula ndi miyalayi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Iye anayankha kuti, “Ine ndikukuwuzani kuti, ngati atakhala chete, miyala idzafuwula.” Onani mutuwo |