Luka 19:39 - Buku Lopatulika39 Ndipo Afarisi ena a m'khamu la anthu anati kwa Iye, Mphunzitsi, dzudzulani ophunzira anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndipo Afarisi ena a m'khamu la anthu anati kwa Iye, Mphunzitsi, dzudzulani ophunzira anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Apo Afarisi ena amene adaali m'khamumo adauza Yesu kuti, “Aphunzitsi, auzeni ophunzira anuŵa aleke zimenezi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Ena mwa Afarisi mʼgulumo anati kwa Yesu, “Aphunzitsi, adzudzuleni ophunzira anu!” Onani mutuwo |