Luka 19:38 - Buku Lopatulika38 nanena, Wolemekezeka Mfumuyo ikudza m'dzina la Ambuye; mtendere mu Mwamba, ndi ulemerero mu Mwambamwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 nanena, Wolemekezeka Mfumuyo ikudza m'dzina la Ambuye; mtendere m'Mwamba, ndi ulemerero m'Mwambamwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Adati, “Ndi yodala Mfumu imene ilikudza m'dzina la Ambuye. Mtendere Kumwamba, ulemu kwa Mulungu kumwambamwamba.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 “Yodala mfumu imene ikubwera mʼdzina la Ambuye!” “Mtendere kumwamba ndi ulemerero mmwambamwamba!” Onani mutuwo |