Luka 19:36 - Buku Lopatulika36 Ndipo pakupita Iye, anayala zovala zao m'njira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Ndipo pakupita Iye, anayala zovala zao m'njira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 Pamene Yesu ankapita, anthu adamchitira ulemu pakuyala zovala zao mu mseu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 Pamene ankapita, anthu anayala zovala zawo mu msewu. Onani mutuwo |