Luka 19:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo anati kwa iye, Mbuye, ali nazo mina khumi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo anati kwa iye, Mbuye, ali nazo mina khumi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 “Iwo adamuyankha kuti, ‘Pepani, ambuye, ameneyu ali kale ndi ndalama makumi khumi.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Iwo anati, “Bwana iyeyu ali nazo kale khumi!” Onani mutuwo |