Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 18:37 - Buku Lopatulika

37 Ndipo anamuuza iye, kuti, Yesu Mnazarayo alinkupita.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Ndipo anamuuza iye, kuti, Yesu Mnazarayo alinkupita.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Adamuyankha kuti, “Kukupita Yesu wa ku Nazarete.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Iwo anamuwuza kuti “Yesu wa ku Nazareti akudutsa.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 18:37
11 Mawu Ofanana  

nadza nakhazikika m'mzinda dzina lake Nazarete kuti chikachitidwe chonenedwa ndi aneneri kuti, Adzatchedwa Mnazarayo.


ndipo pakumva khamu la anthu alinkupita, anafunsa, Ichi nchiyani?


Ndipo anafuula, nanena, Yesu, Mwana wa Davide, mundichitire chifundo.


Ndipo anatsika nao pamodzi nadza ku Nazarete; nawamvera iwo: ndipo amake anasunga zinthu izi zonse mumtima mwake.


Filipo anapeza Natanaele, nanena naye, Iye amene Mose analembera za Iye m'chilamulo, ndi aneneri, tampeza, ndiye Yesu mwana wa Yosefe wa ku Nazarete.


Koma Pilato analemba lembo, naliika pamtanda. Koma panalembedwa, YESU MNAZARAYO, MFUMU YA AYUDA.


Amuna inu Aisraele, mverani mau awa: Yesu Mnazarayo, mwamuna wochokera kwa Mulungu, wosonyezedwa kwa inu ndi zimphamvu, ndi zozizwa, ndi zizindikiro, zimene Mulungu anazichita mwa Iye pakati pa inu monga mudziwa nokha;


zindikirani inu nonse, ndi anthu onse a Israele, kuti m'dzina la Yesu Khristu Mnazarayo, amene inu munampachika pamtanda, amene Mulungu anamuukitsa kwa akufa, mwa Iyeyu munthuyu aimirirapo pamaso panu, wamoyo.


(pakuti anena, M'nyengo yolandiridwa ndinamva iwe, ndipo m'tsiku la chipulumutso ndinakuthandiza. Taonani, tsopano ndiyo nyengo yabwino yolandiridwa, taonani, tsopano ndilo tsiku la chipulumutso);


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa