Luka 18:37 - Buku Lopatulika37 Ndipo anamuuza iye, kuti, Yesu Mnazarayo alinkupita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndipo anamuuza iye, kuti, Yesu Mnazarayo alinkupita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Adamuyankha kuti, “Kukupita Yesu wa ku Nazarete.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Iwo anamuwuza kuti “Yesu wa ku Nazareti akudutsa.” Onani mutuwo |