Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 18:36 - Buku Lopatulika

36 ndipo pakumva khamu la anthu alinkupita, anafunsa, Ichi nchiyani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 ndipo pakumva khamu la anthu alinkupita, anafunsa, Ichi nchiyani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Atamva anthu ambirimbiri akupita mumseumo, adafunsa kuti, “Kodi kuli chiyani?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 anamva gulu la anthu likudutsa. Iye anafunsa chomwe chimachitika.

Onani mutuwo Koperani




Luka 18:36
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anaitana mmodzi wa anyamata, namfunsa, Zinthu izi nzotani?


Ndipo kunali, pamene anayandikira ku Yeriko, msaona wina anakhala m'mbali mwa njira, napemphapempha;


Ndipo anamuuza iye, kuti, Yesu Mnazarayo alinkupita.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa