Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 18:35 - Buku Lopatulika

35 Ndipo kunali, pamene anayandikira ku Yeriko, msaona wina anakhala m'mbali mwa njira, napemphapempha;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

35 Ndipo kunali, pamene anayandikira ku Yeriko, msaona wina anakhala m'mbali mwa njira, napemphapempha;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

35 Pamene Yesu ankayandikira ku Yeriko, munthu wina wakhungu adaakhala pamphepete pa mseu akupemphapempha kwa anthu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

35 Yesu atayandikira ku Yeriko, munthu wina wosaona amene amakhala pambali pa msewu namapempha,

Onani mutuwo Koperani




Luka 18:35
9 Mawu Ofanana  

Ndipo m'kufesa kwake zina zinagwa m'mbali mwa njira, ndipo zinadza mbalame, nkulusira izo.


ndipo pakumva khamu la anthu alinkupita, anafunsa, Ichi nchiyani?


Ndipo analowa, napyola pa Yeriko.


Chifukwa chake anzake ndi iwo adamuona kale, kuti anali wopemphapempha, ananena, Kodi si uyu uja wokhala ndi kupemphapempha?


Ndipo munthu wina wopunduka miyendo chibadwire ananyamulidwa, amene akamuika masiku onse pa khomo la Kachisi lotchedwa Lokongola, kuti apemphe zaulere kwa iwo akulowa mu Kachisi;


Amuutsa waumphawi m'fumbi, nanyamula wosowa padzala, kukamkhalitsa kwa akalonga; ndi kuti akhale nacho cholowa cha chimpando cha ulemerero. Chifukwa nsanamira za dziko lapansi nza Yehova, ndipo Iye anakhazika dziko pa izo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa