Luka 18:35 - Buku Lopatulika35 Ndipo kunali, pamene anayandikira ku Yeriko, msaona wina anakhala m'mbali mwa njira, napemphapempha; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Ndipo kunali, pamene anayandikira ku Yeriko, msaona wina anakhala m'mbali mwa njira, napemphapempha; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Pamene Yesu ankayandikira ku Yeriko, munthu wina wakhungu adaakhala pamphepete pa mseu akupemphapempha kwa anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Yesu atayandikira ku Yeriko, munthu wina wosaona amene amakhala pambali pa msewu namapempha, Onani mutuwo |