Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 18:28 - Buku Lopatulika

28 Ndipo Petro anati, Taonani ife tasiya zathu za ife eni, ndipo takutsatani Inu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

28 Ndipo Petro anati, Taonani ife tasiya zathu za ife eni, ndipo takutsatani Inu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

28 Pamenepo Petro adati, “Ifetu paja tidasiya zonse kuti tizikutsatani.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

28 Petro anati kwa Iye, “Ife tinasiya zonse tinali nazo kutsatira Inu!”

Onani mutuwo Koperani




Luka 18:28
7 Mawu Ofanana  

Pomwepo Petro anayankha, nati kwa Iye, onani, ife tinasiya zonse ndi kutsata Inu; nanga tsono tidzakhala ndi chiyani?


Ndipo Yesu popita, kuchokera kumeneko, anaona munthu, dzina lake Mateyu, alinkukhala polandirira msonkho, nanena kwa iye, Nditsate Ine. Ndipo iye anauka, namtsata.


Petro anayamba kunena naye, Onani, ife tinasiya zonse, ndipo tinakutsatani Inu.


Ndipo m'mene iwo anakocheza ngalawa zao pamtunda, anasiya zonse, namtsata Iye.


Pamene ananena kwa wophunzirayo, Taona, amai wako. Ndipo kuyambira ora lomweli wophunzirayo ananka naye kwao.


Komatu zonse zimene zinandipindulira, zomwezo ndinaziyesa chitayiko chifukwa cha Khristu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa