Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 18:27 - Buku Lopatulika

27 Koma Iye anati, Zinthu zosatheka ndi anthu zitheka ndi Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Koma Iye anati, Zinthu zosatheka ndi anthu zitheka ndi Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Yesu adati, “Zimene zili zosatheka ndi anthu, zimatheka ndi Mulungu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Yesu anayankha kuti, “Zinthu zosatheka ndi anthu zimatheka ndi Mulungu.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 18:27
10 Mawu Ofanana  

Kodi chilipo chinthu chomkanika Yehova? Pa nthawi yoikidwa ndidzabwera kwa iwe, pakufika nyengo yake, ndipo Sara adzakhala ndi mwana wamwamuna.


Ndidziwa kuti mukhoza kuchita zonse, ndi kuti palibe choletsa cholingirira chanu chilichonse.


Ha! Yehova Mulungu, taonani, Inu munalenga kumwamba ndi dziko lapansi ndi mphamvu yanu yaikulu ndi mkono wanu wotambasuka; palibe chokanika Inu;


ndi okhala padziko lapansi onse ayesedwa achabe; ndipo Iye achita mwa chifuniro chake m'khamu la kumwamba ndi mwa okhala padziko lapansi; ndipo palibe woletsa dzanja lake, kapena wakunena naye, Muchitanji?


Atero Yehova wa makamu: Chikakhala chodabwitsa pamaso pa otsala a anthu awa masiku awo, kodi chidzakhalanso chodabwitsa pamaso panga? Ati Yehova wa makamu.


Ndipo Yesu anawayang'ana, nati kwa iwo, Ichi sichitheka ndi anthu, koma zinthu zonse zitheka ndi Mulungu.


Chifukwa palibe mau amodzi akuchokera kwa Mulungu adzakhala opanda mphamvu.


Koma akumvawo anati, Tsono ndani angathe kupulumutsidwa?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa