Luka 18:27 - Buku Lopatulika27 Koma Iye anati, Zinthu zosatheka ndi anthu zitheka ndi Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Koma Iye anati, Zinthu zosatheka ndi anthu zitheka ndi Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Yesu adati, “Zimene zili zosatheka ndi anthu, zimatheka ndi Mulungu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Yesu anayankha kuti, “Zinthu zosatheka ndi anthu zimatheka ndi Mulungu.” Onani mutuwo |