Luka 18:19 - Buku Lopatulika19 Koma Yesu anati kwa iye, Unditcha Ine wabwino bwanji? Palibe wabwino, koma mmodzi, ndiye Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Koma Yesu anati kwa iye, Unditcha Ine wabwino bwanji? Palibe wabwino, koma mmodzi, ndiye Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Yesu adamuyankha kuti, “Ukunditchuliranji wabwino? Wabwinotu ndi mmodzi yekha, Mulungu basi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Yesu anamuyankha kuti, “Chifukwa chiyani ukunditcha wabwino, palibe wabwino kupatula Mulungu yekha. Onani mutuwo |