Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 18:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo anadza nao kwa Iye ana amakanda kuti awakhudze; koma pamene ophunzira anaona anawadzudzula.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo anadza nao kwa Iye ana amakanda kuti awakhudze; koma pamene ophunzira anaona anawadzudzula.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Anthu ena ankabwera ndi ana omwe kwa Yesu kuti aŵakhudze. Ophunzira ake poona zimenezi, ankaŵazazira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Anthu amabweretsanso ana aangʼono kwa Yesu kuti awadalitse. Ophunzira ataona izi, anawadzudzula.

Onani mutuwo Koperani




Luka 18:15
7 Mawu Ofanana  

Koma Yesu anawaitana, nanena, Lolani ana adze kwa Ine, ndipo musawaletse; pakuti Ufumu wa Mulungu uli wa otere.


Ndipo pamene ophunzira ake Yakobo ndi Yohane anaona, anati, Ambuye, Kodi mufuna kuti ife tiuze moto utsike kumwamba ndi kuwanyeketsa iwo?


Ndipo atamletsa kuyamwa anakwera naye, pamodzi ndi ng'ombe ya zaka zitatu, ndi efa wa ufa, ndi thumba la vinyo, nafika naye kunyumba ya Yehova ku Silo; koma mwanayo anali wamng'ono.


Ndipo iwo anapha ng'ombe, nabwera naye mwanayo kwa Eli.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa