Luka 18:12 - Buku Lopatulika12 ndisala chakudya kawiri sabata limodzi; ndipereka limodzi la magawo khumi la zonse ndili nazo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 ndisala chakudya kawiri sabata limodzi; ndipereka limodzi la magawo khumi la zonse ndili nazo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ine ndimasala zakudya kaŵiri pa mlungu, ndipo ndimapereka chachikhumi pa zonse zimene ndimapata.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ine ndimasala kudya kawiri pa Sabata ndipo ndimapereka chakhumi pa zonse ndimapeza.’ Onani mutuwo |