Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 17:35 - Buku Lopatulika

35 Padzakhala akazi awiri akupera pamodzi, mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

35 Padzakhala akazi awiri akupera pamodzi, mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

35 Azimai aŵiri adzakhala akusinja pamodzi, mmodzi adzamtenga, winayo nkumusiya,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

35 Amayi awiri adzakhala pamodzi akusinja; wina adzatengedwa ndi wina adzasiyidwa.

Onani mutuwo Koperani




Luka 17:35
4 Mawu Ofanana  

ndipo ana oyamba a m'dziko la Ejipito adzafa, kuyambira mwana woyamba wa Farao wokhala pa mpando wachifumu wake, kufikira mwana woyamba wa mdzakazi wokhala pa miyala yopera; ndi ana onse oyamba a zoweta.


awiri adzakhala opera pamphero; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa.


Ndinena ndi inu, usiku womwewo adzakhala awiri pa kama mmodzi; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa.


Pamenepo Afilisti anamgwira, namkolowola maso, natsika naye ku Gaza, nammanga ndi maunyolo amkuwa; namperetsa m'kaidi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa