Luka 16:28 - Buku Lopatulika28 pakuti ndili nao abale asanu; awachitire umboni iwo kuti iwonso angadze kumalo ano a mazunzo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 pakuti ndili nao abale asanu; awachitire umboni iwo kuti iwonso angadze kumalo ano a mazunzo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Kumeneko ndili ndi abale anga asanu. Akaŵachenjeze, kuwopa kuti iwonso angabwere ku malo ano amazunzo.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 pakuti ine ndili ndi abale asanu. Lolani iye akawachenjeze kotero kuti asadzabwere kumalo ano amazunzo.’ Onani mutuwo |