Luka 16:27 - Buku Lopatulika27 Koma anati, Pamenepo ndikupemphani, Atate, kuti mumtume kunyumba ya atate wanga; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Koma anati, Pamenepo ndikupemphani, Atate, kuti mumtume kunyumba ya atate wanga; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 “Apo wachuma uja adati, ‘Ndipotu ndikukupemphani atate, kuti mumtume Lazaroyo apite ku nyumba ya bambo wanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 “Iye anayankha kuti, ‘Ndipo ndikupemphani inu, abambo, mutumeni Lazaro ku nyumba ya abambo anga, Onani mutuwo |