Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 16:27 - Buku Lopatulika

27 Koma anati, Pamenepo ndikupemphani, Atate, kuti mumtume kunyumba ya atate wanga;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Koma anati, Pamenepo ndikupemphani, Atate, kuti mumtume kunyumba ya atate wanga;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 “Apo wachuma uja adati, ‘Ndipotu ndikukupemphani atate, kuti mumtume Lazaroyo apite ku nyumba ya bambo wanga.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 “Iye anayankha kuti, ‘Ndipo ndikupemphani inu, abambo, mutumeni Lazaro ku nyumba ya abambo anga,

Onani mutuwo Koperani




Luka 16:27
9 Mawu Ofanana  

Pakuti chomsamalitsa nyumba yake nchiyani, atapita iye, chiwerengo cha miyezi yake chitadulidwa pakati?


Ndipo Yehova anachotsa ukapolo wa Yobu, pamene anapempherera mabwenzi ake; Yehova nachulukitsa zake zonse za Yobu mpaka kuziwirikiza.


kwa anthu, ndi dzanja lanu, Yehova, kwa anthu a dziko lapansi pano amene cholowa chao chili m'moyo uno, ndipo mimba yao muidzaza ndi chuma chanu chobisika; akhuta mtima ndi ana, nasiyira ana amakanda zochuluka zao.


Katsala kanthawi ndipo woipa adzatha psiti; inde, udzayang'anira mbuto yake, nudzapeza palibe.


Njira yao ino ndiyo kupusa kwao, koma akudza m'mbuyo avomereza mau ao.


Potero Mulungu adzakupasula kunthawi zonse, adzakuchotsa nadzakukwatula m'hema mwako, nadzakuzula, kukuchotsa m'dziko la amoyo.


Ndipo ndinada ntchito zanga zonse ndinasauka nazo kunja kuno; pakuti ndidzamsiyira izo munthu wina amene adzanditsata.


Ndipo pamwamba pa izi, pakati pa ife ndi inu pakhazikika phompho lalikulu, kotero kuti iwo akufuna kuoloka kuchokera kuno kunka kwa inu sangathe, kapena kuchokera kwanuko kuyambuka kudza kwa ife, sangathenso.


pakuti ndili nao abale asanu; awachitire umboni iwo kuti iwonso angadze kumalo ano a mazunzo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa