Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 15:31 - Buku Lopatulika

31 Koma iye ananena naye, Mwana wanga, iwe uli ndine nthawi zonse, ndipo zanga zonse zili zako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Koma iye ananena naye, Mwana wanga, iwe uli ndine nthawi zonse, ndipo zanga zonse zili zako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 “Bambo wakeyo adamuyankha kuti, ‘Mwana wanga, iwe uli ndi ine nthaŵi zonse, ndipo zanga zonse nzako.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Abambowo anati, “Mwana wanga, iwe umakhala ndi ine nthawi zonse ndipo zonse ndili nazo ndi zako.

Onani mutuwo Koperani




Luka 15:31
9 Mawu Ofanana  

Koma pamene anadza mwana wanu uyu, wakutha zamoyo zanu ndi akazi achiwerewere, munamphera iye mwanawang'ombe wonenepa.


Koma kudayenera kuti tisangalale ndi kukondwerera: chifukwa mng'ono wako uyu anali wakufa ndipo ali ndi moyo; anatayika, ndipo wapezeka.


Koma kapolo sakhala m'nyumba nthawi yonse; mwana ndiye akhala nthawi yonse.


Chifukwa chake ndinena, Mulungu anataya anthu ake kodi? Msatero ai. Pakuti inenso ndili Mwisraele, wa mbeu ya Abrahamu, wa fuko la Benjamini.


Ndipo anayamba ndani kumpatsa Iye, ndipo adzambwezeranso?


ndiwo Aisraele; ali nao umwana, ndi ulemerero, ndi mapangano, ndi kupatsa kwa malamulo, ndi kutumikira mu Kachisi wa Mulungu, ndi malonjezo;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa