Luka 15:31 - Buku Lopatulika31 Koma iye ananena naye, Mwana wanga, iwe uli ndine nthawi zonse, ndipo zanga zonse zili zako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Koma iye ananena naye, Mwana wanga, iwe uli ndine nthawi zonse, ndipo zanga zonse zili zako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 “Bambo wakeyo adamuyankha kuti, ‘Mwana wanga, iwe uli ndi ine nthaŵi zonse, ndipo zanga zonse nzako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Abambowo anati, “Mwana wanga, iwe umakhala ndi ine nthawi zonse ndipo zonse ndili nazo ndi zako. Onani mutuwo |