Luka 15:28 - Buku Lopatulika28 Koma anakwiya, ndipo sanafune kulowamo. Ndipo atate wake anatuluka namdandaulira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Koma anakwiya, ndipo sanafune kulowamo. Ndipo atate wake anatuluka namdandaulira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Atamva zimenezo mwana wamkuluyo adapsa mtima, nakana kuloŵa. Apo bambo wake adatuluka, nkumupempha mopemba kuti aloŵe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 “Mwana wamkulu anakwiya ndipo anakana kulowa. Chomwecho abambo ake anatuluka ndi kumudandaulira. Onani mutuwo |