Luka 14:32 - Buku Lopatulika32 Koma ngati sakhoza, atumiza akazembe, pokhala winayo ali kutalitali, nafunsa za mtendere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Koma ngati sakhoza, atumiza akazembe, pokhala winayo ali kutalitali, nafunsa za mtendere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Tsono ngati siingathe, idzatuma nthumwi kukapempha mtendere, mfumu ina ija ikali kutali. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Ngati singathe, idzatuma nthumwi pomwe winayo ali kutali ndi kukapempha mgwirizano wamtendere. Onani mutuwo |